1 Chronicles 10:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma anthu a ku Yabesi-Giliyadi atamva zonse zimene Afilisti adaamchita Saulo,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo onse a Yabesi-Giliyadi, atamva zonse Afilisti adachitira Saulo,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene anthu onse okhala ku Yabesi Giliyadi anamva zimene Afilisti anachitira Sauli,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo onse a Yabesi Gileadi, atamva zonse Afilisti adacitira Sauli,