1 Chronicles 12:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina anthu ena a ku Benjamini ndi a ku Yuda adadza ku linga la Davide.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anadza ena a ana a Benjamini ndi Yuda kulinga kwa Davide.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu ena a fuko la Benjamini ndi ena ochokera ku Yuda anabweranso kwa Davide pamene anali ku linga lake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anadza ena a ana a Benjamini ndi Yuda kulinga kwa Davide.