1 Chronicles 12:35 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
A fuko la Dani, anthu 28,600 okonzekera kumenya nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi a Adani akupangira nkhondo zikwi makumi awiri mphambu zisanu ndi zitatu kudza mazana asanu ndi limodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a fuko la Dani, okonzekera nkhondo analipo 28,600.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi a Adani akupangira nkhondo zikwi makumi awiri mphambu zisanu ndi zitatu kudza mazana asanu ndi limodzi.