1 Chronicles 13:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pomwepo Chauta adampsera mtima Uzayo namkantha chifukwa chakuti adatambalitsa dzanja lake nakhudza Bokosi lija. Adafera pomwepo pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi mkwiyo wa Yehova unayakira Uza, namkantha, chifukwa anatambasulira likasa dzanja lake, nafa komweko pamaso pa Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anapsera mtima Uza ndipo anamukantha chifukwa chogwira bokosilo. Choncho iyeyo anafera pomwepo pamaso pa Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi mkwiyo wa Yehova unayakira Uza, namkantha, cifukwa anatambasulira likasa dzanja lace, nafa komweko pamaso pa Mulungu.