1 Chronicles 13:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono atafika ku malo ophunthirapo tirigu ku Kidoni, ng'ombe zidaafuna kugwetsa Bokosi lija, ndiye Uza nkutambalitsa dzanja kuti aligwirire Bokosilo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene anafika ku dwale la Kidoni, Uza anatambasula dzanja lake kulichirikiza likasa, pakuti ng'ombe zikadapulumuka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atafika pa malo opunthira tirigu ku Kidoni, Uza anatambalitsa dzanja lake kuti agwire bokosilo, chifukwa ngʼombe zinkafuna kugwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene anafika ku dwale la Kidoni, Uza anatambasula dzanja lace kulicirikiza likasa, pakuti ng'ombe zikadapulumuka.