1 Chronicles 16:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ongomayendayenda kuchokera ku mtundu wina wa anthu kupita ku mtundu wina, kuchokera ku ufumu wina kupita ku ufumu wina,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nayendayenda kuchokera mtundu wina kufikira mtundu wina, kuchokera ufumu wina kufikira anthu ena.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
iwo anayendayenda kuchoka ku mtundu wina kupita ku mtundu wina, ku ufumu wina kupita ku ufumu wina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nayendayenda kucokera mtundu wina kufikira mtundu wina, Kucokera ufumu wina kufikira anthu ena.