1 Chronicles 16:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Thokozani Chauta, tamandani dzina lake, lalikani za ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yamikani Yehova, itanani dzina lake; bukitsani mwa mitundu ya anthu zochita Iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yamikani Yehova, itanani dzina lake; lalikani za ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yamikani Yehova, itanani dzina lace; Bukitsani mwa mitundu ya anthu zocita iye.