1 Chronicles 17:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malinga ndi zimene tidamva ndi makutu athu, palibenso wina aliyense wonga Inu Chauta, ndipo palibe mulungu wina koma Inu nokha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova, palibe wina wonga inu, palibenso Mulungu wina koma Inu; monga mwa zonse tazimva m'makutu mwathu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Palibe wina wofanana nanu, Inu Yehova, ndipo palibe Mulungu wina koma Inu nokha monga tamvera ndi makutu athu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova, palibe wina wonga inu, palibenso Mulungu wina koma Inu; monga mwa zonse tazimva m'makutu mwathu.