1 Chronicles 17:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma usiku womwewo Chauta adauza Natani kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usiku umenewo mawu a Mulungu anafika kwa Natani, ndipo anati,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,