1 Chronicles 17:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kamuuze mtumiki wanga Davide kuti Ine Chauta ndikuti, Sudzandimangira ndiwe nyumba yoti ndizikhalamo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti, sudzandimangira ndiwe nyumba yokhalamo.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;