1 Chronicles 17:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nchifukwa chake tsono mtumiki wanga Davide umuuze kuti, ‘Chauta Wamphamvuzonse akunena kuti, Ndidakutenga kubusa kumene unkaŵeta nkhosa kuja, kuti udzakhale mfumu yolamulira anthu anga Aisraele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake tsono, uzitero naye mtumiki wanga Davide, Atero Ambuye wa makamu, Ndinakutenga kubusa potsata iwe nkhosa, kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga Israele;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo tsopano umuwuze mtumiki wanga Davide kuti, “Yehova Wamphamvuzonse akuti, Ine ndinakutenga ku busa ukuweta nkhosa, kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga, Aisraeli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace tsono, uzitero naye mtumiki wanga Davide, Atero Ambuye wa makamu, Ndinakutenga kubusa potsata iwe nkhosa, kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga Israyeli;