1 Chronicles 18:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Benaya, mwana wa Yehoyada, anali nduna yoyang'anira Akereti ndi Apeleti. Ndipo ana a Davide anali nduna zazikulu pa ntchito zotumikira mfumu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi Benaya mwana wa Yehoyada anayang'anira Akereti ndi Apeleti; koma ana a Davide ndiwo oyamba ku dzanja la mfumu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Benaya mwana wa Yehoyada anali mtsogoleri wa Akereti ndi Apeleti, ndipo ana a Davide anali alangizi a mfumu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi Benaya mwana wa Yehoyada anayang'anira Akereti ndi Apeleti; koma ana a Davide ndiwo oyamba ku dzanja la mfumu.