1 Chronicles 24:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mbale wake wa Mika anali Isiya. Zekariya anali mdzukulu wa Uziyele, kholo lao linali Isiya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼbale wa Mika: Isiya; kuchokera kwa ana a Isiya: Zekariya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,