1 Chronicles 24:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaŵasankhula pochita maere mosakondera, poti panali atumiki a ku Nyumba ya Chauta ndi atsogoleri achipembedzo pakati pa zidzukulu za Eleazara ndiponso pakati pa zidzukulu za Itamara.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anawagawa ndi maere, awa ndi aja; pakuti panali akalonga a malo opatulika, ndi akalonga a kwa Mulungu, a ana a Eleazara ndi a ana a Itamara omwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anawagawa mosakondera pochita maere, pakuti iwo anali akuluakulu a ku malo opatulika ndi akuluakulu a Mulungu pakati pa zidzukulu za Eliezara ndi Itamara.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anawagawa ndi maere, awa ndi aja; pakuti panali akalonga a malo opatulika, ndi akalonga a kwa Mulungu, a ana a Eleazara ndi a ana a Itamara omwe.