1 Chronicles 27:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Davide sadaŵerengere kumodzi anthu osafika zaka 20 zakubadwa, pakuti Chauta adaalonjeza kuti Aisraele adzachuluka ngati nyenyezi zakumwamba.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Davide sanawerenge iwo a zaka makumi awiri ndi ochepapo, pakuti Yehova adati kuti adzachulukitsa Israele ngati nyenyezi za kuthambo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Davide sanawerenge amuna amene anali ndi zaka makumi awiri kapena kucheperapo, chifukwa Yehova analonjeza kuti adzachulukitsa Aisraeli ngati nyenyezi zamumlengalenga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Davide sanawerenga iwo a zaka makumi awiri ndi ocepapo, pakuti Yehova adati kuti adzacurukitsa Israyeli ngati nyenyezi za kuthambo.