1 Chronicles 28:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Mulungu adandiwuza kuti, ‘Iweyo usati undimangire nyumba, poti iwe ndiwe munthu wankhondo ndipo udakhetsa magazi.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Mulungu anati kwa ine, Sudzamangira dzina langa nyumba, popeza ndiwe munthu wa nkhondo wokhetsa mwazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Mulungu anati kwa ine, “Usandimangire nyumba chifukwa ndiwe munthu wankhondo ndipo wakhala ukukhetsa magazi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Mulungu anati kwa ine, Sudzamangira dzina langa nyumba, popeza ndiwe munthu wa nkhondo wokhetsa mwazi.