1 Chronicles 28:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adandiwuza kuti, ‘Solomoni mwana wako ndiye amene adzamange nyumba yanga ndiponso mabwalo anga. Ndamsankha iyeyo kuti akhale mwana wanga, ndipo Ine ndidzakhala bambo wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati kwa ine, Solomoni mwana wako ndiye adzandimangira nyumba yanga ndi mabwalo anga; pakuti ndamsankha akhale mwana wanga, ndipo Ine ndidzakhala atate wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anati kwa ine, “Solomoni mwana wako ndiye amene adzamanga nyumba yanga ndi mabwalo anga, pakuti Ine ndamusankha kuti akhale mwana wanga ndipo Ine ndidzakhala abambo ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa ine, Solomo mwana wako ndiye adzandimangira nyumba yanga ndi mabwalo anga; pakuti ndamsankha akhale mwana wanga, ndipo Ine ndidzakhala atate wace.