1 Chronicles 29:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta, mukudziŵa kuti ife ndife alendo chabe pansi pano. Tili ngati anthu ongokhala nao chabe, monga momwe analiri makolo athu. Masiku athu okhala pa dziko lapansi ali ngati chithunzithunzi chabe ndipo palibe poti tingakhulupirire.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ife ndife alendo pamaso panu, ndi ogonera, monga makolo athu onse; masiku athu a padziko akunga mthunzi, ndipo palibe kukhalitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ife ndife anthu osadziwika ndiponso alendo pamaso panu, monga analili makolo athu. Masiku anthu pa dziko lapansi ali ngati chithunzithunzi, wopanda chiyembekezo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ife ndife alendo pamaso panu, ndi ogonera, monga makolo athu onse; masiku athu a padziko akunga mthunzi, ndipo palibe kukhalitsa.