1 Chronicles 3:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana aamuna a Yehoyakimu anali aŵa: Yekoniya ndi Zedekiya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi ana a Yehoyakimu: Yekoniya mwana wake, Zedekiya mwana wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Yehoyakimu: Yekoniya ndi Zedekiya mwana wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi ana a Yehoyakimu: Yekoniya mwana wace, Zedekiya mwana wace.