1 Chronicles 4:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Sela, mwana wa Yuda, naŵa: Eri, tate wa Leka, Laada, tate wa Maresa ndi wa mabanja a anthu oomba nsalu zabafuta ku Betasebea.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ana a Sela mwana wa Yuda: Eri atate wa Leka, ndi Laada atate wa Maresa, ndi mabanja a nyumba ya iwo oomba bafuta wa thonje losansitsa a nyumba ya Asibeya,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Sela mwana wa Yuda anali awa: Eri amene anabereka Leka, Laada amene anabereka Maresa ndi mabanja a anthu owomba nsalu zofewa ndi zosalala a ku Beti-Asibeya,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ana a Sela mwana wa Yuda: Eri atate wa Leka, ndi Laada atate wa Maresa, ndi mabanja a nyumba ya iwo oomba bafuta wa thonje losansitsa a nyumba ya Asibeya,