1 Chronicles 6:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo Yehozadaki adagwidwa ukapolo nthaŵi imene Chauta adalola Nebukadinezara kuti agwire ukapolo anthu a ku Yuda ndi a mu Yerusalemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi Yehozadaki analowa undende muja Yehova anatenga ndende Yuda ndi Yerusalemu ndi dzanja la Nebukadinezara.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehozadaki anagwidwa ukapolo pamene Yehova analola Nebukadinezara kuti agwire ukapolo Yuda ndi Yerusalemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi Yehozadaki analowa undende muja Yehova anatenga ndende Yuda ndi Yerusalemu ndi dzanja la Nebukadinezara.