1 Chronicles 6:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Geresomo naŵa: Libini, Yahati ndi Zima,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wa Geresomo: Libini mwana wake, Yahati mwana wake, Zima mwana wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Geresomu ndi awa: Libini, Yehati, Zima,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wa Gerisomu: Libni mwana wace, Yahati mwana wace, Zina mwana wace,