1 Chronicles 6:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Kohati naŵa: Aminadabu, Kora, Asiri,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ana a Kohati: Aminadabu mwana wake, Kora mwana wake, Asiri mwana wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zidzukulu za Kohati ndi izi: Aminadabu, Kora, Asiri,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ana a Kohati: Aminadabu mwana wace, Kora mwana wace, Asiri mwana wace,