1 Chronicles 6:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Panali anthu ena amene Davide adaŵasankhula kuti azitsogolera mwambo wa nyimbo m'Nyumba ya Chauta, ataikamo Bokosi lachipangano.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo aja Davide anawaimika a udindo wa nyimbo m'nyumba ya Yehova, litafikira kupumula likasalo, ndi awa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Awa ndi anthu amene Davide anawayika kuti aziyangʼanira mayimbidwe mʼNyumba ya Yehova, Bokosi la Chipangano litabwera kudzakhala mʼmenemo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo aja Davide anawaimika a udindo wa nyimbo m'nyumba ya Yehova, litafikira kupumula likasalo, ndi awa.