1 Chronicles 6:44 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Etani wa fuko la Merari ankatsogolera gulu lachitatu la oimba. Banja lao likuchokera kwa Levi motere: Etani mwana wa Kisi, mwana wa Abidi, mwana wa Maluki.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi ku dzanja lamanzere abale ao ana a Merari: Etani mwana wa Kisi, mwana wa Abidi, mwana wa Maluki,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo abale awo ena anali a banja la Merari amene amatumikira ku dzanja lake lamanzere: Etani anali mwana wa Kisi, mwana wa Abidi, mwana wa Maluki,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi ku dzanja lamanzere abale ao ana a Merari: Etani mwana wa Kisi, mwana wa Abidi, mwana wa Maluki,