1 Chronicles 6:50 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Aroni ndi zidzukulu zake naŵa: Eleazara, Finehasi, Abisuwa,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ana a Aroni ndiwo Eleazara mwana wake, Finehasi mwana wake, Abisuwa mwana wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Aaroni ndi zidzukulu zake anali awa: Eliezara, Finehasi, Abisuwa,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ana a Aroni ndiwo Eleazara mwana wace, Pinehasi mwana wace, Abisua mwana wace,