1 Chronicles 7:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wa Yediyaele anali Bilihani. Ana a Bilihani naŵa: Yeusi, Benjamini, Ehudi, Kenana, Zetani, Tarisisi ndi Ahisahara.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi mwana wa Yediyaele: Bilihani; ndi ana a Bilihani: Yeusi, ndi Benjamini, ndi Ehudi, ndi Kenana, ndi Zetani, ndi Tarisisi, ndi Ahisahara.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wa Yediaeli anali Bilihani. Ana a Bilihani anali awa: Yeusi, Benjamini, Ehudi, Kenaana, Zetani, Tarisisi ndi Ahisahara.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi mwana wa Yedyaeli: Bilani; ndi ana a Bilani: Yeusi, ndi Benjamini, ndi Ehudi, ndi Kenana, ndi Zetani, ndi Tarasisi, ndi Ahisabara.