1 Chronicles 7:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zidzukulu za Efuremu nazi: Sutela, Beredi, Tahati, Eleada, Tahati,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi ana a Efuremu: Sutela, ndi Beredi mwana wake, ndi Tahati mwana wake, ndi Eleada mwana wake, ndi Tahati mwana wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Efereimu anali awa: Sutela, Beredi, Tahati, Eliada, Tahati,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi ana a Efraimu: Sutera, ndi Beredi mwana wace, ndi Tahati mwana wace, ndi Ekada mwana wace, ndi Tahati mwana wace,