1 Chronicles 8:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Moza adabereka Bineya, Bineya adabereka Rafa, Rafa adabereka Eleasa, Eleasa adabereka Azele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi Moza anabala Bineya, mwana wake ndiye Rafa, mwana wake Eleasa, mwana wake Azele;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Moza anabereka Bineya. Ana ake anali Rafa, Eleasa ndi Azeli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi Moza anabala Bineya, mwana wace ndiye Rafa, mwana wace Eleasa, mwana wace Azeli;