1 Chronicles 9:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
A kwa Alevi naŵa: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, wa kubanja kwa Merari.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi a Alevi: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, a ana a Merari;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Alevi: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, wa mʼbanja la Merari;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi a Alevi: Semaya mwana wal Hasubu, mwana wa Azrikamu, mwana wa Hasabiya, a ana a Merari;