1 Chronicles 9:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Abale ao amene ankakhala nao m'midzi mwao, ankabwera kamodzikamodzi kudzakhala nao masiku asanu ndi aŵiri,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi abale ao m'midzi mwao akafikafika, atapita masiku asanu ndi awiri masabata onse, kuti akhale nao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Abale awo a ku midzi yawo amabwera nthawi ndi nthawi kudzagwira ntchito yawo kwa masiku asanu ndi awiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi abale ao m'midzi mwao akafikafika, atapita masiku asanu ndi awiri masabata onse, kuti akhale nao;