1 Corinthians 1:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero palibe amene anganene kuti adabatizidwa m'dzina langa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti anganene mmodzi kuti mwabatizidwa m'dzina langa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mwakuti palibe amene anganene kuti anabatizidwa mʼdzina langa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti anganene mmodzi kuti mwabatizidwa m'dzina langa.