1 Corinthians 1:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
popeza kuti mau ochitira Khristu umboni akhazikika mwa inu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
monga umboni wa Khristu unakhazikika mwa inu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
chifukwa umboni wathu pa za Khristu unatsimikizidwa mwa inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
mongaumboni wa Kristu unakhazikika mwa inu;