1 Corinthians 10:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero mumtambomo ndi m'nyanjamo onsewo adachita ngati kubatizidwa ndi kukhala amodzi ndi Mose.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nabatizidwa onse kwa Mose, mumtambo, ndi m'nyanja,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo onse anabatizidwa mwa Mose mu mtambo ndi mʼnyanja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nabatizidwa onse kwa Mose, mumtambo, ndi m'nyanja,