1 Corinthians 10:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Osati kuti iweyo ungavutike mu mtima ai, koma iye uja amene wakuuzayo. Pamenepo udzati, “Kodi ufulu wanga utsekerezedwe chifukwa munthu wina mtima wake ukumuvuta?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinena chikumbu mtima, si cha iwe mwini, koma cha winayo; pakuti ufulu wanga uyesedwa ninji ndi chikumbu mtima cha wina?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndikunena za chikumbumtima cha winayo osati chanu. Tsono mungafunse kuti, nʼchifukwa chiyani ufulu wanga ukuphwanyidwa chifukwa cha chikumbumtima cha munthu wina?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinena cikumbu mtima, si ca iwe mwini, koma ca winayo; 1 pakuti ufulu wanga uyesedwa ninji ndi cikumbu mtima ca wina?