1 Corinthians 10:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tisapute Ambuye monga momwe adaaŵaputira ena mwa iwo: paja anthuwo adaphedwa ndi njoka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tisamuyese Khristu, monga ena mwa iwo anachitira ndipo anaphedwa ndi njoka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija.