1 Corinthians 11:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tikadadziyang'ana bwino, sitikadalangidwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ngati tikadadzizindikira tokha sitikadaweruzidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma tikanadziyesa tokha sitikaweruzidwanso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ngati tikadadzizindikira tokha sitikadaweruzidwa.