1 Corinthians 12:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iyai, koma inu muike mtima wanu pa mphatso zopambana. Tsonotu ndikuwonetseni njira yopambana kwenikweni:
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma funitsitsani mphatso zoposa. Ndipo ndikuonetsani njira yokoma yoposatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma funitsitsani mphatso zopambana. Tsopano ndikuonetsani njira yopambana kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma funitsitsani mphatso zoposa. Ndipo ndikuonetsani njira yokoma yoposatu.