1 Corinthians 12:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mzimu Woyera amapatsa munthu aliyense mphatso yakutiyakuti yoti aigwiritse ntchito yopindulitsa anthu onse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma kwa yense kwapatsidwa maonekedwe a Mzimu kuti apindule nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Mzimu amapereka mphatso kwa aliyense kuti ipindulire onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma kwa yense kwapatsidwa maonekedwe a Mzimu kuti apindule nao.