1 Corinthians 14:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wolankhula chilankhulo chosadziŵika, amangothandizidwa yekha, koma wolankhula mau ochokera kwa Mulungu, amathandiza mpingo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amene amayankhula malilime amadzilimbikitsa yekha, koma amene amanenera amalimbikitsa mpingo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.