1 Corinthians 15:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti monga imfa idadza pansi pano kudzera mwa munthu wina, momwemonso kuuka kwa akufa kudadza kudzera mwa munthu wina.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti monga imfa inadza mwa munthu, kuuka kwa akufa kunadzanso mwa munthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti monga imfa inadza kudzera mwa munthu, kuuka kwa akufa kwabweranso kudzera mwa munthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti monga imfa inadza mwa munthu, kuuka kwa akufa kunadzanso mwa munthu.