1 Corinthians 15:38 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Mulungu amaisandutsa mmera monga momwe Iye akufunira, mbeu iliyonse mmera wakutiwakuti.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma Mulungu aipatsa thupi monga afuna; ndi kwa mbeu yonse thupi lakelake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Mulungu amayipatsa thupi monga Iye wafunira, ku mbewu ya mtundu uliwonse amapereka thupi lakelake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma Mulungu iaipatsa thupi mongaafuna; ndi, kwa mbeu yonse thupi lace lace.