1 Corinthians 15:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Potsiriza, pambuyo pa onse adandiwonekeranso ineyo, ngakhale ndili ngati mpolo chabe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo potsiriza pake pa onse, anaoneka kwa inenso monga mtayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Potsiriza pa onse anaonekeranso kwa ine, monga mwana wobadwa nthawi isanakwane.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo potsiriza pace pa onse, anaoneka kwa inenso monga mtayo.