1 Corinthians 16:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngati nkofunika kuti inenso ndipite, tidzapitira limodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati kutaoneka kuti nʼkoyenera kuti ndipite nawo, adzapita nane limodzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane.