1 Corinthians 2:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho pamene ndidafika kwanuko, ndinali wofooka, ndiponso ndinkanjenjemera kwambiri ndi mantha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ine ndinakhala nanu mofooka ndi m'mantha, ndi monthunthumira mwambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinabwera kwa inu wofowoka ndi wamantha, ndiponso wonjenjemera kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ine ndinakhala nanu mofoka ndi m'mantha, ndi monthunthumira mwambiri.