1 Corinthians 4:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzitiwona ngati antchito a Khristu, ngati akapitao osamala zinsinsi za Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chotero munthu atiyese ife, monga atumiki a Khristu, ndi adindo a zinsinsi za Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho tsono anthu atione ife monga atumiki a Khristu, ndiponso ngati osunga zinsinsi za Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cotero munthu atiyese ife, monga atumiki a Kristu, ndi adindo a zinsinsi za Mulungu.