1 Corinthians 4:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikukulemberani zonsezi, osati kuti ndikuchititseni manyazi, koma kuti ndikulangizeni, chifukwa ndinu ana anga okondedwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sindilembera izi kukuchititsani manyazi, koma kuchenjeza inu monga ana anga okondedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sindikulemba izi kuti ndikuchititseni manyazi, koma kukuchenjezani monga ana anga okondedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sindilembera izi kukucititsani manyazi, koma kucenjeza inu monga ana anga okondedwa.