1 Corinthians 4:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikukupemphani tsono kuti muzinditsanzira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ndikupemphani, khalani akutsanza ine.