1 Corinthians 4:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ena mwayamba kudzitukumula, monga ngati sindidzabwerako kwanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ena adzitukumula, monga ngati sindinalinkudza kwa inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ena mwa inu mukudzitukumula, ngati kuti sindingabwere kwanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ena adzitukumula, monga ngati sindinalinkudza kwa inu.