1 Corinthians 4:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti mu Ufumu wa Mulungu chachikulu si mau chabe, koma ntchito.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ufumu wa Mulungu suli m'mau, koma mumphamvu. Mufuna chiyani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti ufumu wa Mulungu si mawu chabe koma mphamvu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ufumu wa Mulungu suli m'mau, koma mumphamvu, Mufuna ciani?